Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Musakachite zimene tikuchita kuno lero, aliyense kumangochita zimene akufuna,+

  • Deuteronomo 28:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 “Ukamveradi mawu a Yehova Mulungu wako mwa kuonetsetsa kuti ukutsatira malamulo ake onse amene ndikukupatsa lero,+ Yehova Mulungu wako adzakukweza ndithu pamwamba pa mitundu yonse ya padziko lapansi.+

  • Oweruza 21:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Masiku amenewo mu Isiraeli munalibe mfumu.+ Aliyense anali kuchita zimene anali kuona kuti n’zoyenera.+

  • Miyambo 14:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pali njira yooneka ngati yowongoka kwa munthu,+ koma mapeto ake ndi imfa.+

  • Miyambo 16:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Njira zonse za munthu zimaoneka zoyera m’maganizo mwake,+ koma Yehova amafufuza zolinga zake.+

  • Miyambo 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Njira iliyonse ya munthu imaoneka yowongoka m’maganizo mwake,+ koma Yehova amafufuza mitima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena