Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 15:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Patapita nthawi Samueli anam’peza Sauli, ndipo Sauli anauza Samueli kuti: “Yehova akudalitseni.+ Ndachita zimene Yehova ananena.”+

  • Salimo 36:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti amadzinyenga yekha,+

      Ndipo sazindikira cholakwa chake ndi kudana nacho.+

  • Miyambo 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Njira iliyonse ya munthu imaoneka yowongoka m’maganizo mwake,+ koma Yehova amafufuza mitima.+

  • Miyambo 30:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pali m’badwo umene umadziona kuti ndi woyera,+ koma sunasambe kuti uchotse ndowe zake.+

  • Yeremiya 17:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Mtima ndi wonyenga kwambiri kuposa china chilichonse ndipo ungathe kuchita china chilichonse choipa.*+ Ndani angaudziwe?

  • Luka 18:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mfarisi uja anaimirira+ ndi kuyamba kupemphera+ mumtima mwake. Iye anati, ‘Mulungu wanga, ndikukuyamikani chifukwa ine sindili ngati anthu enawa ayi. Iwo ndi olanda, osalungama ndi achigololo. Sindilinso ngati wokhometsa msonkho uyu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena