Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 13:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Powatumiza kuti akazonde dziko la Kanani, Mose anawauza kuti: “Pitani ku Negebu,+ ndipo mukafike kudera lamapiri.+

  • Yoswa 2:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tsopano Yoswa mwana wa Nuni anatumiza amuna awiri mwachinsinsi monga azondi kuchokera ku Sitimu.+ Anawalangiza kuti: “Pitani, mukazonde dzikolo ndi mzinda wa Yeriko.” Chotero iwo anapita n’kukafika kunyumba ya mayi wina yemwe anali hule, dzina lake Rahabi,+ n’kukhala kumeneko.

  • Yoswa 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tsopano Yoswa anatumiza amuna ena kuchokera ku Yeriko kupita ku Ai,+ pafupi ndi Beti-aveni,+ kum’mawa kwa Beteli.+ Iye anawauza kuti: “Pitani kumeneko, mukazonde dzikolo.” Amunawo anapita, n’kukazonda dziko la Ai.+

  • Oweruza 1:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pamenepo a nyumba ya Yosefe anayamba kuchita ukazitape+ pamzinda wa Beteli (poyamba dzina la mzindawu linali Luzi).+

  • 1 Samueli 26:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho Davide anatumiza azondi+ kuti akaone ngati Sauli wabweradi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena