Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 13:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Waulesi amalakalaka zinthu, chonsecho moyo wake ulibe chilichonse.+ Koma anthu akhama adzanenepa.+

  • Miyambo 31:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Iye amayang’anira zochitika za pabanja pake, ndipo sadya chakudya cha ulesi.+

  • Miyambo 31:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 M’patseni zipatso za manja ake,+ ndipo ntchito zake zimutamande ngakhale m’zipata.+

  • 1 Atesalonika 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiponso muyesetse kukhala mwamtendere,+ kusalowerera mu nkhani za eni,+ ndi kugwira ntchito ndi manja anu+ monga mmene tinakulamulirani.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena