Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako Boazi anafika kuchokera ku Betelehemu ndipo anauza okololawo kuti: “Yehova akhale nanu.”+ Iwo anayankha mwa nthawi zonse kuti: “Yehova akudalitseni.”+

  • Rute 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Atatero, Boazi anati: “Yehova akudalitse,+ mwana wanga. Kukoma mtima kosatha+ kumene wasonyeza panopa kukuposa koyamba kuja,+ popeza sunafune anyamata, kaya osauka kapena olemera.

  • 2 Samueli 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho Davide anatumiza mithenga kwa amuna a ku Yabesi-giliyadi+ kuti akawauze kuti: “Yehova akudalitseni,+ chifukwa munasonyeza kukoma mtima kosatha+ kwa mbuye wanu Sauli mwa kumuika m’manda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena