Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 9:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iwo anawayankha kuti: “Ee, alipo. Mum’peza kumene mukupitaku. Fulumirani, wafika lero mumzinda chifukwa lero anthu apereka nsembe+ pamalo okwezeka.+

  • 1 Samueli 20:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Anandiuza kuti, ‘Chonde ndilole ndipite kumzinda wakwathu kukapereka nsembe ya banja lathu. M’bale wanga ndi amene wandiitanitsa. Choncho ngati ungandikomere mtima, chonde ndilole ndichoke mwakachetechete ndiponso mofulumira kuti ndikaone abale anga.’ N’chifukwa chake sanabwere kudzadya chakudya pamodzi ndi mfumu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena