Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 22:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 “Usatemberere Mulungu+ kapena kutemberera mtsogoleri amene ali pakati pa anthu ako.+

  • 1 Mbiri 16:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iye anati: ‘Anthu inu musakhudze odzozedwa anga,

      Ndipo aneneri anga musawachitire choipa chilichonse.’+

  • Salimo 105:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye anati: “Anthu inu musakhudze odzozedwa anga,+

      Ndipo aneneri anga musawachitire choipa chilichonse.”+

  • Machitidwe 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pamenepo Paulo anati: “Abale, sindinadziwe kuti ndi mkulu wa ansembe. Pakuti Malemba amati, ‘Wolamulira wa anthu a mtundu wako usamunenere zachipongwe.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena