-
2 Mbiri 20:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Choncho Yehosafati ndi anthu ake anapita kukafunkha+ zinthu zimene adaniwo anali nazo. Iwo anapeza zinthu zochuluka pakati pa anthuwo monga katundu wosiyanasiyana, zovala ndi zinthu zina zabwinozabwino. Chotero anayamba kutenga zinthuzo mpaka zinawakanika kunyamula.+ Kwa masiku atatu anakhala akututa zofunkhazo chifukwa zinalipo zambiri.
-