Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 1:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 n’kuyamba kunena kuti:

      “Ndinatuluka m’mimba mwa mayi anga ndili wamaliseche,+

      Ndipo ndidzabwerera mmenemo ndilinso wamaliseche.+

      Yehova wapereka,+ ndipo Yehova yemweyo watenga.+

      Dzina la Yehova lipitirize kutamandidwa.”+

  • Maliro 3:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Kodi munthu angadandaulirenji+ chifukwa cha zotsatirapo za tchimo lake?+

  • Machitidwe 21:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Titalephera kumusintha maganizo, tinangovomereza ndi kunena kuti: “Chifuniro+ cha Yehova chichitike.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena