Genesis 15:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Pamenepo iye anauza Abulamu kuti: “Unditengere ng’ombe ya zaka zitatu yomwe sinaberekepo, mbuzi yaikazi ya zaka zitatu, nkhosa yamphongo ya zaka zitatu, ndiponso njiwa yaing’ono ndi mwana wa nkhunda.”+ 1 Samueli 6:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Choncho pangani ngolo+ yatsopano, ndipo mutenge ng’ombe ziwiri zoyamwitsa zimene sizinanyamulepo goli+ ndi kuzimangirira kungoloyo. Ana a ng’ombezo muwabweze kunyumba kuti asatsatire amayi awo. 1 Samueli 16:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Koma Samueli anati: “Ndipita bwanji? Sauli akangomva andipha ndithu.”+ Atatero, Yehova anamuuza kuti: “Popita utenge ng’ombe yaikazi yaing’ono pakati pa ng’ombe zako, ndipo ukanene kuti, ‘Ndabwera kudzapereka nsembe kwa Yehova.’+
9 Pamenepo iye anauza Abulamu kuti: “Unditengere ng’ombe ya zaka zitatu yomwe sinaberekepo, mbuzi yaikazi ya zaka zitatu, nkhosa yamphongo ya zaka zitatu, ndiponso njiwa yaing’ono ndi mwana wa nkhunda.”+
7 Choncho pangani ngolo+ yatsopano, ndipo mutenge ng’ombe ziwiri zoyamwitsa zimene sizinanyamulepo goli+ ndi kuzimangirira kungoloyo. Ana a ng’ombezo muwabweze kunyumba kuti asatsatire amayi awo.
2 Koma Samueli anati: “Ndipita bwanji? Sauli akangomva andipha ndithu.”+ Atatero, Yehova anamuuza kuti: “Popita utenge ng’ombe yaikazi yaing’ono pakati pa ng’ombe zako, ndipo ukanene kuti, ‘Ndabwera kudzapereka nsembe kwa Yehova.’+