Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Nthawi ina, Samisoni anapita ku Gaza+ ndipo anaona hule kumeneko ndi kulowa m’nyumba ya huleyo.+

  • Oweruza 16:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chotero Afilisiti anam’gwira ndi kum’boola maso+ n’kupita naye ku Gaza.+ Anam’manga ndi zomangira ziwiri zamkuwa,+ ndipo anakhala woyendetsa mwala wa mphero+ m’ndende.+

  • Amosi 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndidzatumiza moto pakhoma la Gaza+ ndipo udzanyeketsa nsanja zake zokhalamo.

  • Machitidwe 8:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Koma mngelo wa Yehova+ analankhula kwa Filipo kuti: “Nyamuka ndi kulowera kum’mwera, kumsewu wochokera ku Yerusalemu kupita ku Gaza.” (Umenewu ndi msewu wa m’chipululu.)

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena