Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mngelo wa Yehova atalankhula mawu amenewa kwa ana onse a Isiraeli, anthuwo anayamba kulira mokweza mawu.+

  • Nehemiya 9:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 “Koma akangokhala pa mtendere, anali kuchitanso zoipa pamaso panu+ ndipo munali kuwasiya m’manja mwa adani awo amene anali kuwapondaponda.+ Zikatero, anali kubweranso kwa inu ndi kupempha thandizo lanu,+ ndipo inu munali kumva muli kumwambako+ ndi kuwapulumutsa mobwerezabwereza, chifukwa cha chifundo chanu chachikulu.+

  • 2 Akorinto 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kumva chisoni mogwirizana ndi chifuniro cha Mulungu kumachititsa munthu kulapa ndi kupeza chipulumutso, zimene munthu sangadandaule nazo.+ Koma chisoni cha dziko chimabweretsa imfa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena