Levitiko 20:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 N’chifukwa chake ndinakuuzani+ kuti: “Inuyo mudzatenga dzikolo ndipo ine ndidzalipereka m’manja mwanu kuti likhale lanu, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndakupatulani kwa anthu a mitundu ina.”+ Numeri 23:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Pakuti pomwe ndili pano ndikutha kuwaona, pamwamba pa matanthwe pano,Ndikuwaona ndithu, pano pamwamba pa mapiri.Akukhala paokhaokha m’mahema awo,+Iwo akudziona kuti ndi osiyana ndi mitundu ina.+ Deuteronomo 7:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pakuti ndinu anthu oyera kwa Yehova Mulungu wanu.+ Yehova Mulungu wanu anakusankhani kuti mukhale anthu ake, chuma chake chapadera, mwa anthu onse okhala padziko lapansi.+ 1 Samueli 8:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Atafika kumeneko anamuuza kuti: “Iweyo wakalamba, koma ana ako sakutsatira chitsanzo chako. Ndiye tikufuna kuti utiikire mfumu+ yoti izitiweruza ngati mitundu ina yonse.” Salimo 106:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Iwo anayamba kusakanikirana ndi mitundu ina,+Ndi kuyamba kuphunzira zochita zawo.+
24 N’chifukwa chake ndinakuuzani+ kuti: “Inuyo mudzatenga dzikolo ndipo ine ndidzalipereka m’manja mwanu kuti likhale lanu, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndakupatulani kwa anthu a mitundu ina.”+
9 Pakuti pomwe ndili pano ndikutha kuwaona, pamwamba pa matanthwe pano,Ndikuwaona ndithu, pano pamwamba pa mapiri.Akukhala paokhaokha m’mahema awo,+Iwo akudziona kuti ndi osiyana ndi mitundu ina.+
6 Pakuti ndinu anthu oyera kwa Yehova Mulungu wanu.+ Yehova Mulungu wanu anakusankhani kuti mukhale anthu ake, chuma chake chapadera, mwa anthu onse okhala padziko lapansi.+
5 Atafika kumeneko anamuuza kuti: “Iweyo wakalamba, koma ana ako sakutsatira chitsanzo chako. Ndiye tikufuna kuti utiikire mfumu+ yoti izitiweruza ngati mitundu ina yonse.”