-
Oweruza 21:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Ndipo ana a Isiraeli anayamba kumva chisoni chifukwa cha Benjamini m’bale wawo. Choncho anati: “Lero fuko limodzi ladulidwa ndi kuchotsedwa mu Isiraeli.
-