Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Chotero, Yehova anamva chisoni+ kuti anapanga anthu padziko lapansi, ndipo zinam’pweteka kwambiri mumtima.+

  • 1 Samueli 15:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Samueli anamuyankha kuti: “Sindibwerera nawe chifukwa wakana mawu a Yehova, ndipo Yehova wakukana kuti upitirize kukhala mfumu ya Isiraeli.”+

  • 1 Samueli 15:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Samueli analirira+ Sauli ndipo sanaonanenso naye mpaka tsiku la imfa yake. Koma Yehova anamva chisoni kuti anaika Sauli kukhala mfumu ya Isiraeli.+

  • Yeremiya 18:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 ndiyeno anthuwo n’kusiya zoipa zimene anali kuchita, zimene ndinawadzudzula nazo,+ pamenepo ndidzasintha maganizo anga kuti ndisawagwetsere tsoka limene ndinafuna kuwagwetsera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena