Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Patapita nthawi, Adoniya mwana wa Hagiti anapita kwa Bati-seba,+ amayi a Solomo. Iwo atamuona, anam’funsa kuti: “Kodi mwabwerera mtendere?”+ Iye anayankha kuti: “Inde, ndabwerera mtendere.”

  • 2 Mafumu 9:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Yehoramu atangoona Yehu, nthawi yomweyo anam’funsa kuti: “Kodi ukubwerera zamtendere Yehu?” Koma Yehu anayankha kuti: “Mtendere ungakhalepo bwanji+ pali dama la Yezebeli+ mayi ako ndi amatsenga ake ambirimbiri?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena