Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 48:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Yehova wanena kuti, “Oipa alibe mtendere.”+

  • Yesaya 57:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Oipa alibe mtendere,”+ akutero Mulungu wanga.

  • Yesaya 59:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Iwo amangonyalanyaza njira yamtendere,+ ndipo m’njira zawo mulibe chilungamo.+ Misewu yawo aikhotetsakhotetsa.+ Palibe munthu aliyense woyenda mmenemo amene adzadziwe mtendere.+

  • Yeremiya 16:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Yehova wanena kuti, ‘Usalowe m’nyumba imene olira maliro akuchitiramo phwando, ndipo usapite kukalira nawo maliro kapena kuwamvera chisoni.’+

      “‘Pakuti anthu awa ndawachotsera mtendere wanga, kukoma mtima kosatha ndi chifundo,’+ watero Yehova.

  • Aroma 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 ndipo sadziwa njira ya mtendere.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena