Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 59:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choonadi chikusowa+ ndipo aliyense wokana zoipa akusakazidwa.+

      Yehova anaona zimenezi ndipo zinamuipira m’maso mwake poona kuti panalibe chilungamo.+

  • Amosi 6:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “‘Kodi mahatchi angathamange pathanthwe, kapena kodi munthu angalime pathanthwe ndi ng’ombe? Anthu inu mwakana chilungamo,+ choncho mwachititsa moyo wa anthu kukhala wowawa.

  • Habakuku 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 “Choncho lamulo latha mphamvu ndipo anthu sakuchitanso chilungamo.+ Chilungamo chapotozedwa chifukwa anthu oipa akupondereza anthu olungama.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena