Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 12:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mahema a anthu olanda amakhala opanda nkhawa,+

      Ndipo anthu okwiyitsa Mulungu amakhala pa mtendere

      Wofanana ndi wa munthu amene watenga mulungu* m’manja mwake.+

  • Salimo 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Anthu oipa akuyendayenda ponseponse,

      Chifukwa ana a anthu amayamikira zoipa.+

  • Mlaliki 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Popeza anthu ochita zoipa sanalangidwe msanga,+ n’chifukwa chake mtima wa ana a anthu wakhazikika pa kuchita zoipa.+

  • Mateyu 23:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Tsoka kwa inu alembi ndi Afarisi, onyenga inu! Chifukwa mumapereka chakhumi+ cha timbewu ta minti, dilili, ndi chitowe, koma mumanyalanyaza zinthu zofunika za m’Chilamulo, monga chilungamo,+ chifundo+ ndi kukhulupirika.+ Kupereka zinthu zimenezi n’kofunikadi, koma osanyalanyaza zinthu zinazo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena