Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 8:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Farao ataona kuti mliri wa achulewo watha, anaumitsa mtima wake,+ ndipo sanamvere Mose ndi Aroni, monga momwe Yehova ananenera.+

  • 1 Samueli 2:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndipo iye anali kuwauza kuti:+ “Mukuchitiranji zinthu zoterezi?+ Chifukwatu anthu onse akundiuza zinthu zoipa zokhazokha zokhudza inu.+

  • Salimo 10:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mumtima mwake amanena kuti: “Sindidzagwedezeka.+

      Palibe chimene chidzandichitikira ku mibadwomibadwo.”+

  • Yesaya 26:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ngakhale munthu woipa atachitiridwa zabwino, sangaphunzire chilungamo.+ M’dziko lochita zowongoka, iye adzachita zinthu zopanda chilungamo+ ndipo sadzaona ukulu wa Yehova.+

  • Mateyu 24:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 “Koma ngati kapolo woipayo anganene mumtima mwake+ kuti, ‘Mbuye wanga akuchedwa,’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena