Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 8:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Farao ataona kuti mliri wa achulewo watha, anaumitsa mtima wake,+ ndipo sanamvere Mose ndi Aroni, monga momwe Yehova ananenera.+

  • Salimo 106:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Nthawi zambiri anali kuwalanditsa,+

      Koma iwo anali kumupandukira chifukwa sanali kumumvera,+

      Ndipo anali kuwatsitsa chifukwa cha zolakwa zawo.+

  • Miyambo 1:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Pakuti kupanduka+ kwa osadziwa n’kumene kudzawaphe+ ndipo mphwayi za opusa n’zimene zidzawawononge.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena