Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 16:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 “Uza khamulo kuti, ‘Chokani kumahema a Kora, Datani ndi Abiramu!’”+

  • Yoswa 7:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Dzuka! Yeretsa anthuwa,+ uwauze kuti, ‘Mawa mudziyeretse, pakuti Yehova, Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti: “Kalanga Isiraeli, pakati panu pali zinthu zoyenera kuwonongedwa.+ Anthu inu simudzathanso kulimbana ndi adani anu, kufikira mutachotsa pakati panu zinthu zoyenera kuwonongedwazo.

  • Miyambo 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Woipa amangofunafuna kupanduka,+ ndipo munthu amene watumidwa kuti akamulange sam’chitira chifundo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena