Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 40:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mkwiyo wako wosefukira utuluke,+

      Ndipo uone aliyense wodzikweza n’kumutsitsa.

  • Salimo 18:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Chifukwa anthu osautsika mudzawapulumutsa,+

      Koma anthu odzikweza mudzawatsitsa.+

  • Salimo 101:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Aliyense wonenera mnzake miseche,+

      Ndimamukhalitsa chete.+

      Sindingathe kupirira zochita za+

      Aliyense wodzikweza ndi wamtima wonyada.+

  • Danieli 4:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 “Tsopano ine Nebukadinezara ndikutamanda, kukweza ndi kulemekeza Mfumu yakumwamba,+ chifukwa ntchito zake zonse ndizo choonadi, njira zake ndi zolungama,+ ndiponso amatha kutsitsa anthu onyada.”+

  • 1 Petulo 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chimodzimodzinso inu anyamata. Muzigonjera+ amuna achikulire. Koma nonsenu muzichitirana zinthu modzichepetsa,+ chifukwa Mulungu amatsutsa odzikweza, koma odzichepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena