Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 78:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Anawasonyeza mkwiyo wake woyaka moto,+

      Ukali, ziweruzo zamphamvu ndi masautso.+

      Anawatumizira makamu a angelo obweretsa masoka.+

  • Salimo 90:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndani angadziwe kukula kwa ukali wanu,+

      Ndi kukula kwa mkwiyo wanu kumene kumafanana ndi ulemu umene muyenera kulandira?+

  • Yeremiya 30:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Taonani! Mphepo yamkuntho yochokera kwa Yehova yawomba. Mkwiyo wake wawomba ngati kamvulumvulu wosakaza.+ Wawomba pamitu ya anthu oipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena