Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Kondwerani, mitundu inu, pamodzi ndi anthu ake,+

      Pakuti adzabwezera magazi a atumiki ake,+

      Ndipo adzabwezera chilango kwa adani ake,+

      Nadzaphimba machimo a dziko la anthu ake.”

  • Salimo 18:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 N’chifukwa chake ndidzakutamandani, inu Yehova pakati pa mitundu.+

      Ndipo ndidzaimba nyimbo zotamanda dzina lanu.+

  • Salimo 117:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 117 Tamandani Yehova, inu mitundu yonse ya anthu.+

      Mulemekezeni, inu mafuko onse.+

  • Aroma 15:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 kuti mitundu ina+ ipereke ulemerero kwa Mulungu chifukwa cha chifundo+ chake, monga mmene Malemba amanenera kuti: “N’chifukwa chake ndidzakuvomerezani poyera pakati pa mitundu. Ndipo ndidzaimba nyimbo zotamanda dzina lanu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena