Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 43:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Yuda anauza bambo ake kuti:+ “Munthu ujatu anatichenjeza mwamphamvu kuti, ‘Musadzayese n’komwe kuonekeranso pamaso panga mukadzalephera kubwera naye m’bale wanuyo.’+

  • Genesis 44:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Koma ife tinati, ‘Sitingathe kutsikira kumeneko. Ngati tikhala naye limodzi mng’ono wathuyu tipitako, chifukwa sitingathe kukaonekeranso pamaso pa munthuyo tikapanda kupita naye.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena