Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 40:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamene Mose anali kuutsa chihema chopatulikacho, anayala pansi zitsulo zake zamphako+ ndi kukhazikapo mafelemu.+ Ndiyeno analowetsa mitengo yake yonyamulira+ ndi kuimika mizati pamalo ake.+

  • Ekisodo 40:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Pamenepo mtambo+ unayamba kuphimba chihema chokumanako, ndipo ulemerero wa Yehova unadzaza m’chihemacho.

  • 1 Mbiri 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kuchokera tsiku limene ndinatulutsa Isiraeli mu Iguputo kufikira lero,+ sindinakhalepo m’nyumba, koma ndakhala m’hema ndi m’hema ndiponso m’chihema chopatulika+ ndi m’chihema chopatulika.+

  • Machitidwe 7:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 “Makolo athuwo anali ndi chihema cha umboni m’chipululu. Anachipanga potsatira malangizo amene Mulungu anapereka pamene anali kulankhula ndi Mose. Mulungu anauza Mose kuti apange chihemacho molingana ndi chithunzi chimene anachiona.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena