Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 3:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 ‘Yehova Ambuye Wamkulu Koposa, inu ndinu amene mwayamba kuchititsa atumiki anu kuti aone ukulu wanu+ ndi dzanja lanu lamphamvu.+ Ndi mulungu winanso uti, kumwamba kapena padziko lapansi, amene akuchita ntchito ngati zanu, ndiponso ntchito zamphamvu ngati zanu?+

  • 1 Mbiri 16:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pakuti Yehova ndi wamkulu ndi woyenera kutamandidwa kwambiri,+

      Ndipo ndi woyenera kuopedwa kuposa milungu ina yonse.+

  • Salimo 86:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti inu ndinu wamkulu ndipo mukuchita zinthu zodabwitsa.+

      Inu nokha ndinu Mulungu.+

  • Salimo 96:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Pakuti Yehova ndi wamkulu+ ndi woyenera kutamandidwa kwambiri.

      Iye ndi wochititsa mantha kuposa milungu ina yonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena