Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 14:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho pa tsiku la 7, Samisoni asanalowe m’chipinda cha mkaziyo,+ amuna a mumzindawo anamuuza kuti:

      “Kodi chokoma kuposa uchi n’chiyani,

      Ndipo champhamvu kuposa mkango n’chiyani?”+

      Poyankha iye anawauza kuti:

      “Mukanapanda kulima ndi ng’ombe yanga yaikazi,+

      Simukanatha kumasulira mwambi wanga.”+

  • Miyambo 30:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Mkango, umene ndi wamphamvu kwambiri panyama zonse zakutchire ndiponso umene suopa chilichonse n’kubwerera m’mbuyo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena