Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 23:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Taonani, mtundu udzadzuka ngati mkango,

      Udzanyamuka monga mkango.+

      Sugona pansi mpaka ugwire nyama,

      Ndipo udzamwa magazi a ophedwawo.”+

  • Oweruza 14:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pamenepo Samisoni anapita ku Timuna+ pamodzi ndi bambo ndi mayi ake. Atafika m’minda ya mpesa ya ku Timuna, anakumana ndi mkango wamphamvu umene unayamba kubangula utamuona.

  • Oweruza 14:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho pa tsiku la 7, Samisoni asanalowe m’chipinda cha mkaziyo,+ amuna a mumzindawo anamuuza kuti:

      “Kodi chokoma kuposa uchi n’chiyani,

      Ndipo champhamvu kuposa mkango n’chiyani?”+

      Poyankha iye anawauza kuti:

      “Mukanapanda kulima ndi ng’ombe yanga yaikazi,+

      Simukanatha kumasulira mwambi wanga.”+

  • Yesaya 31:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pakuti Yehova wandiuza kuti: “Mkango umalira moopseza, ngakhale mkango wamphamvu,+ poteteza nyama imene wagwira. Abusa ambirimbiri akaitanidwa kuti adzauthamangitse, ngakhale umve mawu awo suchita mantha ndipo ngakhale azichita phokoso suopa. M’njira yomweyo, Yehova wa makamu adzatsika kuti achite nkhondo poteteza phiri la Ziyoni ndiponso poteteza phiri lake laling’ono.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena