Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno Davide ananena kuti: “Kodi pali aliyense wotsala wa m’nyumba ya Sauli? Ndikufuna kumusonyeza kukoma mtima kosatha+ chifukwa cha Yonatani.”+

  • 2 Samueli 16:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako mfumu inauza Ziba kuti: “Taona, zonse zimene zinali za Mefiboseti+ ndi zako.” Pamenepo Ziba anati: “Ndikuwerama+ pamaso panu. Pitirizani kundikomera mtima mbuyanga mfumu.”

  • 2 Samueli 19:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Komabe mfumu inamuuza kuti: “N’chifukwa chiyani ukupitiriza kulankhula zonsezi? Ine ndikuti, iwe ndi Ziba mugawane mundawo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena