Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 22:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamenepo bambo ndi mayi a mtsikanayo azibweretsa umboni wosonyeza kuti mtsikanayo anali namwali kwa akulu a mzinda kuchipata cha mzindawo.+

  • Deuteronomo 25:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Ngati mwamunayo sakufuna kutenga mkazi wamasiye wa m’bale wakeyo, mkaziyo azinyamuka ndi kupita kuchipata kwa akulu+ ndi kuwauza kuti, ‘M’bale wa mwamuna wanga wakana kusunga dzina la m’bale wake mu Isiraeli. Sanavomereze kuchita ukwati wa pachilamu ndi ine.’

  • Rute 4:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Zitatero, Boazi anapita kuchipata.+ Kumeneko iye anakhala pansi. Ali chikhalire choncho, anaona wowombola anam’tchula uja+ akudutsa. Ndiyeno Boazi anati: “Iwe Uje takhotera pano, khala pansi apa.” Motero anakhota n’kukhala pansi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena