Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma atumiki+ a Yehoasi anagwirizana zom’chitira chiwembu+ ndipo anamupha panyumba+ ya Chimulu cha Dothi*+ panjira yotsetserekera ku Sila.

  • 2 Mafumu 17:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Koma mfumu ya Asuri inaona kuti Hoshiya anali kuichitira chiwembu,+ chifukwa chakuti iye anatumiza amithenga kwa So mfumu ya Iguputo,+ ndiponso sanapereke msonkho kwa mfumu ya Asuri monga anali kuchitira zaka zam’mbuyo. Choncho mfumu ya Asuri inam’manga n’kumutsekera m’ndende.+

  • 2 Mbiri 25:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Amaziya atasiya kutsatira Yehova, anthu anam’konzera chiwembu+ ku Yerusalemu. Patapita nthawi iye anathawira ku Lakisi.+ Koma anthuwo anatumiza anthu ena omwe anamutsatira ku Lakisiko n’kukamuphera komweko.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena