Salimo 41:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Koma munthu amene ndinali kukhala naye mwamtendere, amene ndinali kumukhulupirira,+Munthu amene anali kudya chakudya changa,+ wakweza chidendene chake kundiukira.+ Salimo 55:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Pakuti amene ananditonza si mdani.+Akanakhala mdani ndikanapirira.Amene anadzikweza pamaso panga si munthu wodana nane kwambiri.+Akanakhala munthu wodana nane kwambiri ndikanabisala.+ Mateyu 26:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 n’kuwafunsa kuti: “Kodi mudzandipatsa chiyani ndikamupereka kwa inu?”+ Iwo anamulonjeza ndalama 30 zasiliva.+ Yohane 13:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Sindikunena nonsenu, ndikudziwa amene ndawasankha.+ Koma zili choncho kuti Malemba akwaniritsidwe,+ paja amati, ‘Munthu amene anali kudya chakudya changa wanyamula chidendene chake kundiukira.’+
9 Koma munthu amene ndinali kukhala naye mwamtendere, amene ndinali kumukhulupirira,+Munthu amene anali kudya chakudya changa,+ wakweza chidendene chake kundiukira.+
12 Pakuti amene ananditonza si mdani.+Akanakhala mdani ndikanapirira.Amene anadzikweza pamaso panga si munthu wodana nane kwambiri.+Akanakhala munthu wodana nane kwambiri ndikanabisala.+
15 n’kuwafunsa kuti: “Kodi mudzandipatsa chiyani ndikamupereka kwa inu?”+ Iwo anamulonjeza ndalama 30 zasiliva.+
18 Sindikunena nonsenu, ndikudziwa amene ndawasankha.+ Koma zili choncho kuti Malemba akwaniritsidwe,+ paja amati, ‘Munthu amene anali kudya chakudya changa wanyamula chidendene chake kundiukira.’+