Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 3:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Abineri atabwerera ku Heburoni,+ Yowabu anam’tengera pambali kuchipata kuti alankhulane naye pa awiri.+ Koma kumeneko anamubaya pamimba+ moti anafa chifukwa chokhetsa magazi a Asaheli,+ m’bale wake wa Yowabu.

  • 2 Samueli 23:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Asaheli+ m’bale wake wa Yowabu anali m’gulu la amuna 30 aja. M’gululi munalinso Elihanani+ mwana wa Dodo wa ku Betelehemu,

  • 1 Mbiri 11:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Amuna amphamvu a magulu ankhondo anali Asaheli+ m’bale wake wa Yowabu, Elihanani+ mwana wa Dodo wa ku Betelehemu,

  • 1 Mbiri 27:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mtsogoleri wachinayi, wa mwezi wachinayi, anali Asaheli+ m’bale wake wa Yowabu,+ ndipo mwana wake Zebadiya anabwera pambuyo pake. Gulu lake linali ndi anthu 24,000.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena