Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 18:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Chotero Abulahamu anathamangira kwa Sara n’kumuuza kuti: “Fulumira! Tenga ufa wosalala wokwana miyezo itatu ya seya,* uukande, ndipo upange makeke ozungulira.”+

  • 1 Samueli 28:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano mkaziyo anali ndi mwana wa ng’ombe wonenepa+ m’nyumba yake. Choncho anam’pereka nsembe msangamsanga,+ ndipo anatenga ufa n’kuukanda ndi kuphika mikate yopanda chofufumitsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena