Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 11:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndiyeno Yehova anamuyankha Mose kuti: “Kodi dzanja la Yehova lafupika lero eti?+ Tsopano uona ngati zimene ndanena zichitikedi kapena ayi.”+

  • Oweruza 15:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Chotero Mulungu anang’amba nthaka ku Lehi ndipo madzi+ anayamba kutuluka panthakapo. Pamenepo Samisoni anamwa madziwo, moti anapezanso mphamvu+ ndi kutsitsimulidwa.+ N’chifukwa chake anatcha malowo kuti Eni-hakore.* Malo amenewa ali ku Lehi kufikira lero.

  • Salimo 37:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pa nthawi yatsoka sadzachita manyazi,+

      Ndipo pa nthawi ya njala adzakhuta.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena