Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 26:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Anthu asanu mwa inu adzathamangitsa adani 100, ndipo anthu 100 adzathamangitsa adani 10,000, moti mudzagonjetsa adani anu ndi lupanga.+

  • Deuteronomo 28:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Yehova adzachititsa adani ako amene adzakuukira kugonja pamaso pako.+ Pobwera kwa iwe adzadutsa njira imodzi, koma pothawa pamaso pako, adzadutsa njira 7.+

  • Salimo 33:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Palibe mfumu imene inapulumuka chifukwa cha kukula kwa gulu lake lankhondo.+

      Munthu wamphamvu sapulumuka chifukwa cha kuchuluka kwa mphamvu zake.+

  • Salimo 46:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mitundu ya anthu inachita phokoso,+ maufumu anagwedezeka.

      Iye anatulutsa mawu ndipo dziko lapansi linasungunuka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena