Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 29:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ndiyeno Afilisiti+ anasonkhanitsa asilikali awo onse ku Afeki, pamene Aisiraeli anamanga msasa pafupi ndi kasupe amene anali ku Yezereeli.+

  • 2 Mafumu 13:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako Elisa anati: “Tsegulani windo lakum’mawa.” Iye analitsegula. Ndiyeno Elisa anati: “Ponyani muviwo!” Choncho iye anauponya. Tsopano Elisa anati: “Muvi wa Yehova wopulumutsa! Muvi wopulumutsa+ kwa Asiriya! Ndithu mudzapha Asiriya ku Afeki+ mpaka kuwamaliza.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena