Yoswa 4:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Pa tsikuli, Yehova anachititsa Yoswa kukhala wamkulu m’maso mwa Aisiraeli onse,+ ndipo anayamba kumuopa monga mmene anaopera Mose masiku onse a moyo wake.+ 1 Samueli 12:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Choncho Samueli anafuulira Yehova,+ moti Yehova anadzetsa mabingu ndi mvula tsiku limenelo.+ Pamenepo anthu onse anachita mantha kwambiri ndi Yehova ndiponso ndi Samueli. 1 Mbiri 29:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Akalonga onse+ ndi amuna amphamvu,+ ndiponso ana onse a Mfumu Davide,+ anali kugonjera Solomo mfumu. Salimo 72:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Iwo adzakuopani nthawi zonse pamene dzuwa likuwala,+Adzakuopani ku mibadwomibadwo pamene mwezi uli kuthambo.+ Miyambo 24:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Mwana wanga uziopa Yehova ndiponso mfumu.+ Usamakhale pagulu la anthu ofuna kuti zinthu zisinthe,+
14 Pa tsikuli, Yehova anachititsa Yoswa kukhala wamkulu m’maso mwa Aisiraeli onse,+ ndipo anayamba kumuopa monga mmene anaopera Mose masiku onse a moyo wake.+
18 Choncho Samueli anafuulira Yehova,+ moti Yehova anadzetsa mabingu ndi mvula tsiku limenelo.+ Pamenepo anthu onse anachita mantha kwambiri ndi Yehova ndiponso ndi Samueli.
24 Akalonga onse+ ndi amuna amphamvu,+ ndiponso ana onse a Mfumu Davide,+ anali kugonjera Solomo mfumu.
5 Iwo adzakuopani nthawi zonse pamene dzuwa likuwala,+Adzakuopani ku mibadwomibadwo pamene mwezi uli kuthambo.+
21 Mwana wanga uziopa Yehova ndiponso mfumu.+ Usamakhale pagulu la anthu ofuna kuti zinthu zisinthe,+