Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Khonde+ la kutsogolo kwa chipinda chachikulu* cha nyumbayo linali mikono 20 m’litali, kufanana ndi m’lifupi mwa nyumbayo. Khondelo linali kutsogolo kwa nyumbayo, ndipo linali mikono 10 m’lifupi mwake.

  • 1 Mafumu 7:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kuzungulira bwalo lalikulu panali khoma la miyala yosema lotalika mizere itatu+ kuchokera pansi, ndi mzere umodzi wa matabwa a mkungudza pamwamba pake. Bwalo lamkati+ la nyumba+ ya Yehova ndi khonde+ la nyumbayo, zinamangidwanso mofanana.

  • Ezekieli 40:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Kenako ananditengera pakhonde la nyumbayo.+ Pamenepo anayeza chipilala cham’mbali cha khondelo ndipo anapeza kuti chinali mikono isanu mbali iyi ndi mikono isanu mbali inayo. M’lifupi mwa khomo la nyumbayo munali mikono itatu mbali iyi ndi mikono itatu mbali inayo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena