Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 14:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Iye anali kugulula mawilo a magaleta awo moti anali kuwayendetsa movutikira.+ Pamenepo Aiguputo anayamba kunena kuti: “Tiyeni tithawe pamaso pa Isiraeli, chifukwa Yehova akuwamenyera nkhondo yolimbana ndi Aiguputo.”+

  • Yesaya 5:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Mivi yawo ndi yakuthwa ndipo mauta awo onse ndi okungika.+ Ziboda za mahatchi awo n’zolimba ngati mwala wa nsangalabwi.+ Mawilo a magaleta awo ali ngati mphepo yamkuntho.+

  • Yesaya 28:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pakuti anthu sapuntha chitowe chakuda ndi chida chopunthira+ ndipo pachitowe chamtundu wina sayendetsapo mawilo a ngolo yopunthira mbewu. Nthawi zambiri chitowe chakuda amachipuntha ndi ndodo+ ndipo chitowe chamtundu wina amachipuntha ndi kamtengo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena