Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 5:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno Yehova anapatsa Solomo nzeru monga mmene anam’lonjezera.+ Pakati pa Hiramu ndi Solomo panali mtendere, ndipo awiriwa anachita pangano.

  • 1 Mafumu 22:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Panali pa nthawi imeneyo pamene Ahaziya mwana wa Ahabu anapempha Yehosafati kuti: “Bwanji antchito anga apite pamodzi ndi antchito anu m’zombozo?” Koma Yehosafati anakana.+

  • 2 Mbiri 8:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Hiramu,+ kudzera mwa antchito ake, ankatumizira Solomo zombo ndi antchito odziwa za panyanja.+ Iwo ankapita ku Ofiri+ pamodzi ndi antchito a Solomo kukatenga golide+ wokwana matalente* 450,+ ndipo anali kubwera naye kwa Mfumu Solomo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena