-
Ezara 9:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Choncho musakapereke ana anu aakazi kwa ana awo aamuna,+ kapena kutenga ana awo aakazi n’kuwapereka kwa ana anu aamuna. Ndipo mpaka kalekale, musakawathandize kukhala ndi mtendere+ ndiponso kutukuka. Mukachite zimenezi kuti mukakhale amphamvu+ ndiponso kuti mukadyedi zabwino za dzikolo ndi kulitengadi kuti likhale la ana anu mpaka kalekale.’+
-