Oweruza 1:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Pa nthawi imeneyi, nawonso a nyumba ya Yosefe+ anapita kukamenyana ndi mzinda wa Beteli,+ ndipo Yehova anali nawo.+ 2 Samueli 19:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Pakuti ine mtumiki wanu ndikudziwa bwino kuti ndinachimwa. Tsopano lero ndine woyamba m’nyumba yonse ya Yosefe+ kubwera kuno kudzakumana ndi inu mbuyanga mfumu.” Amosi 5:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Yesetsani kuyandikira kwa Yehova, inu a m’nyumba ya Yosefe,+ kuti mupitirize kukhala ndi moyo+ ndiponso kuti Mulungu asakuyakireni ngati moto.+ Chitani zimenezi kuti motowo usakunyeketseni chifukwa ku Beteli sikungapezeke munthu wouzimitsa.+
22 Pa nthawi imeneyi, nawonso a nyumba ya Yosefe+ anapita kukamenyana ndi mzinda wa Beteli,+ ndipo Yehova anali nawo.+
20 Pakuti ine mtumiki wanu ndikudziwa bwino kuti ndinachimwa. Tsopano lero ndine woyamba m’nyumba yonse ya Yosefe+ kubwera kuno kudzakumana ndi inu mbuyanga mfumu.”
6 Yesetsani kuyandikira kwa Yehova, inu a m’nyumba ya Yosefe,+ kuti mupitirize kukhala ndi moyo+ ndiponso kuti Mulungu asakuyakireni ngati moto.+ Chitani zimenezi kuti motowo usakunyeketseni chifukwa ku Beteli sikungapezeke munthu wouzimitsa.+