Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 22:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Pa nthawi ya zowawa zanga ndinaitana Yehova,+

      Ndinaitana Mulungu wanga.+

      Pamenepo iye anamva mawu anga ali m’kachisi wake,+

      Makutu ake anamva kulira kwanga kopempha thandizo.+

  • 2 Mbiri 20:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 ‘Likatigwera tsoka,+ lupanga, chiweruzo chowawa, mliri+ kapena njala,+ tiziima pamaso pa nyumba iyi+ ndi pamaso panu (popeza dzina lanu+ lili m’nyumba iyi), kuti tifuulire inu kuti mutithandize m’masautso athu, ndipo inu muzimva ndi kutipulumutsa.’+

  • Yobu 5:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Adzakulanditsa m’masautso 6,+

      Ndipo m’masautso 7, palibe choipa chimene chidzakukhudze.+

  • Hoseya 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako ndidzabwerera kumalo anga kufikira iwo atalangidwa chifukwa cha zolakwa zawo+ ndipo adzayamba kufunafuna nkhope yanga.+ Zinthu zikadzawavuta,+ adzandifuna.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena