Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 71:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Inenso ndidzakutamandani ndi chipangizo cha zingwe,+

      Ndidzatamanda choonadi chanu, inu Mulungu.+

      Ndidzaimba nyimbo zokutamandani ndi zeze, Inu Woyera wa Isiraeli.+

  • Salimo 89:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pakuti chishango chathu ndi chochokera kwa Yehova,+

      Ndipo mfumu yathu ndi yochokera kwa Woyera wa Isiraeli.+

  • Yeremiya 51:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Pakuti Mulungu, Yehova wa makamu,+ sanasiye Isiraeli ndi Yuda+ kuti akhale mkazi wamasiye. Dziko la Akasidi lili ndi mlandu waukulu pamaso pa Woyera wa Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena