Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 M’njira zonse za Yehova muli kukoma mtima kosatha ndi choonadi

      Kwa anthu osunga pangano+ lake ndi zikumbutso zake.+

  • Salimo 108:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Pakuti kukoma mtima kwanu kosatha n’kwakukulu ndipo kwafika kumwamba,+

      Choonadi chanu chafika kuthambo.+

  • Salimo 138:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndidzawerama nditayang’ana kukachisi wanu woyera,+

      Ndipo ndidzatamanda dzina lanu+

      Chifukwa cha kukoma mtima kwanu kosatha+ ndi choonadi chanu.+

      Pakuti malonjezo+ amene munawachita m’dzina lanu ndi aakulu ndithu. Koma kukwaniritsidwa kwa malonjezowo n’kwakukulu koposa.+

  • Salimo 146:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Wopanga kumwamba ndi dziko lapansi,+

      Nyanja ndi zonse zili mmenemo.+

      Wosunga choonadi mpaka kalekale.+

  • Chivumbulutso 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iwo akuimba nyimbo ya Mose+ kapolo wa Mulungu, ndi nyimbo ya Mwanawankhosa,+ yakuti:

      “Ntchito zanu n’zazikulu ndi zodabwitsa,+ inu Yehova Mulungu Wamphamvuyonse.+ Njira zanu ndi zolungama ndi zoona,+ inu Mfumu yamuyaya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena