Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndi mulungu wina uti amene angafanane nanu, inu Yehova?+

      Ndinu woyera kopambana, ndani angafanane ndi inu?+

      Ndinu woyenera kuopedwa+ ndi kukuimbirani nyimbo zotamanda.+ Inu ndinu wochita zodabwitsa.+

  • Salimo 92:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ntchito zanu ndi zazikuludi inu Yehova!+

      Maganizo anu ndi ozama kwambiri.+

  • Salimo 111:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ntchito za Yehova ndi zazikulu,+

      ד [Daʹleth]

      Onse amene amasangalala nazo amazisinkhasinkha.+

  • Salimo 139:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndidzakutamandani chifukwa munandipanga modabwitsa ndipo zimenezi zimandichititsa mantha.+

      Ntchito zanu ndi zodabwitsa,+

      Ndipo ine ndimadziwa bwino zimenezi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena