Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 15:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma m’badwo wachinayi udzabwerera kuno,+ chifukwa nthawi yoti Aamori alangidwe sinakwane.”+

  • Levitiko 18:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndiye chifukwa chake dzikolo n’lodetsedwa, ndipo ndidzalilanga chifukwa cha kulakwa kwake. Pamenepo dzikolo lidzataya anthu ake kunja.+

  • Ezekieli 16:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Umuuze kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, akunena kwa iwe Yerusalemu kuti: “Iwe unachokera kudziko la Akanani ndipo unabadwira komweko.+ Bambo ako anali Muamori,+ mayi ako anali Mhiti.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena